Chichewa
stringlengths 10
500
| emotion
stringclasses 7
values |
---|---|
Kenako tinaona kalavani inayake yakutha.
|
disgust
|
Ndikuganiza kuti ukunena zowona, Aaron.
|
neutral
|
"Ndipo akutiponyera fanizo (lotsutsa kukhoza Kwathu kuukitsa akufa) ndi kuiwala chilengedwe chake (chochokera kumadzi opanda pake).
|
disgust
|
Koma dziwani izi: Mukandipha, mudzakhala mukupha munthu wosalakwa.'
|
anger
|
Kodi nanunso mwapeza zomwe Mbuye wanu adakulonjezani kuti nzoona?"
|
neutral
|
"Koma amene angafune (zina) kusiya zimenezi iwowo ndiwo olumpha malire.
|
disgust
|
Tipatsirenitu gawo la chilango chathu lisanafike tsiku lachiwerengero."
|
anger
|
Ndipo akakapempha chithandizo (chifukwa cha ludzu loopsya lomwe likawapeza), akathandizidwa popatsidwa madzi (otentha kwambiri) monga madzi a chitsulo chosungunuka, omwe adzasupula nkhope zawo.
|
disgust
|
Pakuti dzanja lanu linali kundilemera usana ndi usiku."
|
fear
|
Yemwe angakhale connected ndi Qur'an, akhala wolemekezeka kuposa wina aliyense, chifukwa Allah analemekeza chilichonse chokhudzana ndi Qur'an.
|
neutral
|
Ndipo posachedwa adzawalipira pa zomwe adali kupeka.
|
anger
|
Kumbukirani kuti analemba kuti: "Mulungu ali wamkulu woposa mitima yathu."
|
neutral
|
Pamapeto pa tsiku, banja liyenera kuiwala zonse - a Mark V. Olson.
|
sadness
|
"Kodi akukulonjezani kuti mukadzafa ndikusanduka dothi ndi mafupa, mudzaukitsidwanso (m'manda)?
|
disgust
|
Ndiye dzifunseni kuti, 'Kodi n'kutheka kuti Mulungu akugwiritsa ntchito anthu amenewa pofuna kundikokera kwa iye?'
|
neutral
|
"Sipadzakhala (china) koma mkuwe umodzi basi; adzangozindikira iwo onse atabweretsedwa patsogolo Pathu.
|
neutral
|
Iye anati: "Ndachita pangano ndi maso anga.
|
neutral
|
Kodi kunyumba kwa bambo ako kuli malo oti tikhoza kugonako?"
|
neutral
|
ndipo wolungama akhale motetezedwa.
|
neutral
|
Nena: "Zozizwitsa zili kwa Allah; ndipo ine ndine mchenjezi woonekera, (ndilibe mphamvu zokudzetserani zozizwitsa koma pokhapo Allah atafuna)."
|
neutral
|
Ndipo wawaikira nthawi (yodziwika) yopanda chikaiko, (yowaukitsira ku imfa).
|
sadness
|
"Kodi zidzakhala zotani pamene tidzawasonkhanitsa tsiku lopanda chikaiko?
|
neutral
|
"Kapena iwo ali nawo othandidzana nawo (pa mau awa)?
|
neutral
|
Onse adzabwerera kwa Ife.
|
neutral
|
Adzabwerera tsiku la nkhondo.
|
neutral
|
Ndipo amene atembenukire kutali (kunyoza iwe, ndiye kuti zoipa zili pa iye mwini).
|
anger
|
" (Nena:) "Kodi ndifune woweruza wina kusiya Allah, pomwe Iye ndi Yemwe adavumbulutsa buku kwa inu lofotokoza chilichonse?"
|
fear
|
"Kuti liwachenjeze amene ali moyo, ndi kuti litsimikizike liwu (la chilango) pa osakhulupirira.
|
fear
|
Ndipo anthu untamed adzalowa izo, ndipo iwo aiipitse.
|
disgust
|
"Basi, kumbutsa (anthu) ndithu iwe, ndiwe mkumbutsi.
|
neutral
|
Komabe, "ikapezedwa idzabwezera kasanu ndi kaŵiri; idzapereka chuma chonse cha m'nyumba yake."
|
anger
|
Zinali zosatheka, zinali m'magazi anga.
|
surprise
|
Kodi munthu akuganiza kuti Ife (Amene tidamlenga kuchokera Popanda chilichonse) sitidzatha Kusonkhanitsa mafupa ake (ofumbwa)?
|
disgust
|
"Ndipo ndithu alipo ena mwa inu otsalira m'mbuyo sapita ku nkhondo, (ndiponso amaletsa anzawo).
|
neutral
|
"Naipereka kwa iwo (koma sadadye); iye adanena (modabwa): "Kodi bwanji simukudya?"
|
anger
|
"Ndithu Ine ndine Allah palibe wopembedzedwa mwachoonadi koma Ine; choncho ndipembeze, pemphera Swala moyenera pondikumbukira.
|
joy
|
Ndipo mwaphunzitsidwa (ndi iyi Qur'an) zomwe simudali kuzidziwa, inu ngakhale makolo anu.
|
neutral
|
Ndiyendetseni m'njira yoona,
|
neutral
|
Koma osadandaula, Lena, zomwe ndidakwanitsabe kuwombera.
|
fear
|
Pakuti ndaona kuti mukhale basi pamaso panga, mkati m'badwo uno.
|
anger
|
Davide anali ndi zinthu zonsezi koma anakhala wodzichepetsa kwa moyo wake wonse.
|
neutral
|
Kapena yochokera Dead kapena Alive.
|
neutral
|
"Ndipo iwo akadakhulupirira nadzitchinjiriza (ku zoletsedwa), ndithudi, mphoto yochokera kwa Allah ikadakhala yabwino kwa iwo, akadadziwa.
|
neutral
|
Unali wangwiro m'njira zako chilengedwere iwe, mpaka chinapezeka mwa iwe chosalungama.
|
anger
|
Koma popeza pa nthawiyi n'kuti dzina la Mulungu likudziwika kale, n'chifukwa chiyani Mose anafunsa funso limeneli?
|
neutral
|
"Ndithu amene adzadze kwa Mbuye wake uku ali wamachimo, adzapeza moto wa Jahannam; sadzafa m'menemo, ndipo sadzakhalanso ndi moyo wabwino.
|
sadness
|
Kodi ukuona chifukwa chake Mulungu anawononga anthuwo? - Iwo anali oipa, ndipo zimene ankaganiza zinali 'zoipa zokhazokha.'
|
disgust
|
"Akukufunsa za mowa ndi njuga.
|
neutral
|
Cifukwa cace, taonani, nditumiza kwa inu aneneri ndi anzeru ndi alembi.
|
neutral
|
"Adati: "Sichina ichi (Qur'an) koma ndi matsenga amene adalandiridwa (kuchokera kwa amatsenga akale),
|
neutral
|
mu maina Ake Iye Wapamwambamwamba,
|
disgust
|
Ngati akadamumvera Allah, ndithu zikadakhala zabwino kwa iwo.
|
neutral
|
"Auze amene sadakhulupirire: "Posachedwapa mugonjetsedwa ndi kusonkhanitsidwa ndi kuponyedwa ku Moto.
|
fear
|
Iye anayankha kuti: "Inde, ndifedi Akristu chifukwa chakuti Yesu ndiye chitsanzo chathu.
|
neutral
|
Taonani, adzailowa kwa inu, ndipo mudzaona njira yawo ndi zimene anachita.
|
neutral
|
"M'nthaka muli zizindikiro kwa otsimikiza, (zosonyeza kuti Allah alipo).
|
neutral
|
""Pita ndi kalata yangayi, kaiponye kwa iwo; kenako ukadzipatule kwa iwo (ukakhale pambali) ndi kuona momwe azikayankhira."
|
neutral
|
Tsoka inu, chifukwa muli ngati manda achikumbutso osaonekera, moti anthu amayenda pamwamba pake koma osadziwa!"
|
disgust
|
Ngati utsata zilakolako zawo pambuyo pa zomwe zakudzera, monga kuzindikira (kwenikweni), sudzapeza mtetezi aliyense ngakhale mthandizi kwa Allah.
|
neutral
|
Panopa Satana akuukira kwambiri anthu a Mulungu.
|
disgust
|
(Akawauza kuti): "Ndithu iyi ndi mphoto
|
joy
|
Ndipo kum'bandakucha, iwo Amapempha chikhululuko.
|
sadness
|
Tikatero, mnzathuyo sadzavutika kutimvetsera.
|
neutral
|
Ndipo pamene mukuwapatsa chuma chawo, funani mboni (zoonelera kuperekedwa kwa chumacho).
|
anger
|
"Komanso wochitira zabwino makolo ake ndipo sadali wodzitukumula (kwa anthu) kapena kunyoza (Allah).
|
neutral
|
"Choncho apewe (osakhulupirirawa) amene anyozera chikumbutso Chathu (Qur'an); ndipo palibe chimene akufuna koma moyo wa padziko lapansi basi.
|
neutral
|
Sindinawauze amayi ako zokwanira; Ndikanayenera kumamuuza tsiku lililonse chifukwa anali wangwiro tsiku lililonse.
|
neutral
|
Nena: "Nanga bwanji simukumuopa?"
|
fear
|
Mtima wake wakhazikika, sadzaopa, kufikira adzaona adani ake.
|
fear
|
Perekani chitsanzo cha "zakuya za Mulungu" zomwe gulu la kapolo lazifotokoza.
|
neutral
|
Kapena kudza zina mwa zizindikiro za Mbuye wako (zomwe adati zidzadza)?
|
neutral
|
"Ndipo adatuluka kuchipinda chopemphelera ndikuonekera kwa anthu ake, ndipo adawalozera (pomwe sadathe kuyankhula) kuti: "Lemekezani Allah m'mawa ndi madzulo."
|
neutral
|
""Ndipo Allah achilimbikitsa choonadi ndi mau Ake, ngakhale oipa anyansidwe nazo."
|
anger
|
Mtsikana akhoza kukhala ndipo adzatchedwa yemweyo - Nastya.
|
neutral
|
pa dziko ndithudi umenewo ukuchokera kwa Iye Subhaanahu Wataalaa.
|
neutral
|
Kodi iwe ukuganiza kuti mwa aŵiriŵa ndani anasangalatsa Mulungu?
|
neutral
|
Ndimasulireni maloto angawa, ngati inu mumatha kumasulira maloto."
|
neutral
|
"Ena mwa inu mwawawona kale 'alonda athu apamwamba' kale.
|
neutral
|
""Ndithu takhulupirira Mbuye wathu kuti atikhululukire zolakwa zathu ndi matsenga amene watikakamiza (kuchita); ndipo Allah ndi Yemwe ali Wabwino ndi Wamuyaya (osati iwe)."
|
neutral
|
Ndipo taika chidani ndi kusakondana pakati pawo mpaka tsiku la chimariziro.
|
anger
|
Ngati anamva zimenezi Dhamma, adzakhala ndi mwamsanga anamvetsa izo.'
|
neutral
|
"Kodi sadaone kuti (mwana wang'ombe) sabweza mawu kwa iwo, ndiponso sangathe kudzetsa matsautso kwa iwo ngakhale zothandiza.
|
disgust
|
Mngelo amene analankhula ndi Yosefe anati: "Adzapulumutsa anthu ake ku machimo awo."
|
neutral
|
""Ndipo tikukhazikani (inu) pambuyo pawo m'dzikomo.
|
neutral
|
Limatiuza dzina la mkazi wake ndiponso mayina a ena mwa ana ake.
|
neutral
|
Ndipo chikadza chipulumutso chochokera kwa Mbuye wako amanena: "Ndithu ife tidali pamodzi ndi inu."
|
neutral
|
kwa anthu a dziko lino amene mphotho yawo ili mʼmoyo uno.
|
joy
|
Koma chofunika kwambiri n'chakuti zimene tinkachita pa nthawiyi zinathandiza kuti tilimbitse ubwenzi wathu ndi Mulungu komanso kuti ine ndi mkazi wanga tizigwirizana kwambiri."
|
neutral
|
"Nena: "Kodi nthaka njayani ndi zomwe zili m'menemo, ngati inu mukudziwa (kanthu)!"
|
neutral
|
Izo ndi zosangalatsa za moyo wa dziko lapansi (zomwe sizili kanthu).
|
joy
|
Ndipo kodi njokayo ndi ndaninso yoti n'kukayikira chilungamo cha mawu a Mulungu ndi mawu a mwamuna wake?
|
disgust
|
Solomo anali ndi chuma kuposa anthu onse a m'mbuyo mwake.
|
neutral
|
koma nyanga za olungama zidzakwezedwa.
|
anger
|
Mumampempha modzichepetsa ndi motsitsa mawu (kuti): "Ngati atipulumutsa m'mazunzo awa, ndithudi tidzakhala mwa othokoza."
|
neutral
|
Koma Yesu ali padzikoli analamula kuti: "Lekani kuweruza poona maonekedwe akunja, koma muziweruza ndi chiweruzo cholungama."
|
anger
|
Iye anawayika chitonzo chamuyaya.
|
disgust
|
Kenaka anawapatsa ulamuliro kulakhula ngati kuti ndi mwini wake akulakhual.
|
anger
|
"E inu ana a Israyeli! kumbukirani chisomo Changa chomwe ndidakudalitsani nacho, ndipo kwaniritsani pangano Langa Nanenso ndikwaniritsi pangano lanu.
|
neutral
|
Ndipo sadzapeza mthandizi ndi mtetezi kupatula Allah.
|
neutral
|
Bambo wako sadali munthu woipa, ngakhalenso mayi wako sadali wachiwerewere."
|
disgust
|
Subsets and Splits
No community queries yet
The top public SQL queries from the community will appear here once available.