Chichewa
stringlengths 10
500
| emotion
stringclasses 7
values |
---|---|
Kukanidwa alibe phindu pa tsiku limenelo.
|
neutral
|
Ndipo aliyense sadziwa chomwe apeze mawa; (chabwino kapena choipa); ndiponso sadziwa aliyense kuti ndi dziko liti adzafera.
|
neutral
|
""Kodi mukudabwa kukudzerani ulaliki wochokera kwa Mbuye wanu kudzera mwa munthu wa mwa inu, (yemwe wadza) kuti akuchenjezeni ndi kuti muope (Allah), ndikutinso muchitiridwe chifundo?"
|
surprise
|
Inu sadzamva ana akuseka ndi kusewera mu Gehena, chifukwa palibe ana mu gehena.
|
disgust
|
Ndipo mwa inu amene akhalepo (pa mudzi) m'mweziwu, asale.
|
neutral
|
Ndiyeno anayamba kuuzana kuti: "Sitili kuchita bwino ife; tsiku lino ndilo tsiku la uthenga wabwino."
|
sadness
|
Zimenezo nchifukwa chakuti iwo adatsutsa zizindikiro Zathu ndipo anali osazilabadira.
|
disgust
|
Koma angakhale akukondabe Mulungu mumtima mwawo.
|
neutral
|
Aleke asangalale (ndi zoipa zawozo); posachedwa adzadziwa.
|
joy
|
mau powerenga Quràn, ndipo mosakhala m'menemo adzanong'ona powerenga.
|
neutral
|
Iye alonga: 'Iwo ndiwo mbumba yakuipa yakuti nkhabe bvera miyambo yanu.
|
anger
|
Ndipo iye ndi wopunduka diso lakumanja,
|
neutral
|
Tiyeni timgulitse iye kwa Aismayele, tisasamulire iye manja; chifukwa ndiye mbale wathu, thupi athu.
|
anger
|
mkazi wopanda ana, ngati mtengo wopanda nthambi;
|
disgust
|
Mulungu adati kwa Yobu, "Kodi udali kuti pamene ine ndinkayika madziko a dziko lapansi?
|
neutral
|
ku chilango cha tsiku limenelo ndi ana ake.
|
disgust
|
ndi kuti ukawayankhe zoona amene akutumawo?
|
neutral
|
Lero ndi tsiku lomwe muyenera kuyendera San Marino: The ...
|
neutral
|
"Ndipo mumpingo uliwonse tidzatulutsa mboni (yawo yowaikira umboni), ndipo tidzawauza: "Bwerani ndi umboni wanu."
|
neutral
|
Komatu nyumba ya chimaliziro idzawakhalira bwino amene akuopa (Allah).
|
joy
|
Ngati ukundiona ine kuti ndili ndi chuma chochepa ndi ana ochepa kuposa iwe (koma sindisiya kutamanda Allah)."
|
neutral
|
Ndipo amene angamphatikize Allah, ndithudi, wadzipekera uchimo waukulu.
|
disgust
|
"Sadzalawa imfa mmenemo, kupatula imfa yoyamba ija; ndipo adzawateteza kuchilango cha Jahena,
|
sadness
|
"Ndipo woipa adzauona moto (panthawi imeneyo) ndikutsimikiza kuti iwo alowa m'menemo.
|
sadness
|
"Kodi nchiyani chakupezani (kuti muweruze mopanda chilungamo); nanga mukuweruza bwanji (zimenezi)?
|
neutral
|
Kodi wadya zipatso za mtengo uja umene ndinakulamula kuti usadye? "
|
disgust
|
Sindinamvepo za inu anyamata, Ndinu ndani padziko lapansi?
|
surprise
|
Kodi sindiyenera kumvera chisoni mzinda waukulu ngati uwu?"
|
sadness
|
Koma Allah akunena choona; Iye akuongolera ku njira yoongoka.
|
neutral
|
Ambiri anazindikira kuti iye ankaphunzitsa choonadi ndipo "anakhala okhulupirira."
|
neutral
|
Ndipo adzawalowetsa m'minda yomwe pansi pake pakuyenda mitsinje, adzakhala m'menemo muyaya.
|
neutral
|
Tsopano zakhala ngati nyumba yachiwiri, ndimakonda kukakhala ku Dubai.
|
joy
|
"Ndipo musakhale monga aja amene adagawikana nasiyana pambuyo powadzera zisonyezo zoonekera poyera (zowaletsa kutero).
|
neutral
|
"Ngati atafuna angakuchotseni ndi kubweretsa zolengedwa zatsopano.
|
neutral
|
Ndipo kotero muwaike iwo pansi - ndipo mochuluka kwambiri.
|
neutral
|
Akanachokanso, mwina si bwenzi pano ndili m'gulu la Yehova."
|
neutral
|
Koma akadachita zomwe auzidwa, zikadakhala zabwino kwa iwo.
|
neutral
|
Kodi n'ciyani comwe cidacitika pomwe Salomau alibe kubvera cenjezo la Mulungu?
|
fear
|
Ndipo nyumba iliyonse yomwe apezako wampatuko, aziigwetsa."
|
anger
|
" (Iwo) adati: "Ndithu ife kwa Mbuye wathu ngobwerera."
|
neutral
|
"Ndipo tidampulumutsa iye ndi Luti kupita ku dziko lomwe tidalidalitsa ku zolengedwa.
|
joy
|
"Kuti achitsimikizire choonadi ndi kulichotsa bodza; ngakhale zikuwaipira anthu oipa.
|
disgust
|
Kudziwa zinthu ndi kuzindikira kumatuluka m'kamwa mwake."
|
neutral
|
Ale anaibva, anapulumuka.
|
neutral
|
Anthu akhoza kutiuza kuti: "Anthufe timafunika kusangalala ndi moyo.
|
joy
|
Adalitsike Yehova, amene wapumulitsa anthu ake Israyeli, monga mwa zonse adalonjeza: sanataya mawu amodzi m'zonse zabwino zomwe adalonjeza ndi dzanja la Mose mtumiki wake.
|
neutral
|
Choncho padziko panali magulu a anthu awiri; omwe anali kupembedza Allah Subhaanah wa Ta'ala, ndi ena omwe anali kupitiriza kupembedza mafano.
|
neutral
|
Choncho pamene adamdzera, (mneneri Shuaib) ndikumulongosolera nkhani, adati: "Usaope; wapulumuka kwa anthu oipa."
|
fear
|
Pamene anali kuvutika, sanawopseze, koma anali kudzipereka kwa iye amene amaweruza molungama."
|
fear
|
Iye anati: "Ndinatsatira malangizo amene akulu anandipatsa ndipo ndinayamba moyo wosalira zambiri.
|
neutral
|
Ngati ndati ayi, ndiye kuti ndili wotanganidwa.
|
sadness
|
Mtima wake udzakwezeka, ndipo adzagwetsa anthu masauzande ambiri; koma sadzakhala wamphamvu. "
|
sadness
|
Koma masiku ano tili pafupi kwambiri ndi nthawi imene Mulungu akufuna kukwaniritsa zimene analonjeza.
|
joy
|
"Ndipo ndithu Ife ndi Wokhoza kukuonetsa (chilango) chimene tikuwalonjeza.
|
neutral
|
"Kenako akadzafuna adzamuukitsa (pambuyo pa imfa).
|
disgust
|
Ine ndidzalanga dziko chifukwa zoipa zake, oipa chifukwa cha kusaweruzika kwawo.
|
anger
|
Palibe kumene kuli malipiro anga koma kwa Mbuye wa zolengedwa."
|
neutral
|
Ndipo m'zimenezi choonadi chakufika ndi ulaliki ndiponso chikumbutso kwa okhulupirira.
|
neutral
|
Kwenikweni, zomwe amaphunzitsa ndi chowonadi cha Mulungu mpaka atatiuza mosiyana.
|
neutral
|
Iwowo ndiomwe Allah sadafune kuyeretsa mitima yawo.
|
neutral
|
Mukabisale kumeneko masiku atatu, mpaka iwo atabwerako, kenako muzikapita kwanu."
|
neutral
|
Ndithu m'zimenezi muli zisonyezo kwa anthu anzeru.
|
neutral
|
Ndipo taikonza Jahannam kukhala ndende ya osakhulupirira."
|
neutral
|
Mulungu anapanga pangano ndi ife.
|
neutral
|
Bambo wako sadali munthu woipa, ngakhalenso mayi wako sadali wachiwerewere,"
|
disgust
|
"Amene amaimilira kupemphera napereka chimene tawapatsa, (pa njira ya Allah, ndikuthandiza ovutika).
|
neutral
|
owongoka (ofotokoza za choona).
|
neutral
|
Ndipo anapitadi kumwamba mu mtambo adani awo aja akuwaona.
|
anger
|
Komanso oitanidwa aja, amene ali osankhidwa mwapadera ndi okhulupirika, nawonso adzagonjetsa naye limodzi."
|
neutral
|
Choncho, adzaiitana koma siidzawayankha; ndipo tidzaika chionongeko pakati pawo (ndipo sadzakumananso).
|
sadness
|
Iye anati: "Inu ndinu mchere wa dziko lapansi.
|
disgust
|
Anadzipangira yekha kudzathandiza tsiku lina, ngati angathe.
|
neutral
|
Ine sinditsata china koma zomwe zikuvumbulutsidwa kwa ine."
|
neutral
|
Adzabwera ndi mthenga wa pangano amene mukumuyembekezera mosangalala."
|
neutral
|
"Kwa Iye ndiko kuli (kuvomera) pempho lachoonadi.
|
neutral
|
Nthaŵi zonse angelo anali kudziŵa kumene Paulo anali, ndipo anamuthandiza.
|
neutral
|
"Chifukwa chakuchita kwawo zoipa, awo Ayuda, tidaletsa kwa iwo zinthu zabwino (zakudya) zomwe zidali zovomerezeka kwa iwo; ndiponso chifukwa cha kutsekereza kwawo anthu ambiri kuyenda panjira ya Allah.
|
disgust
|
Koma chifukwa cha osankhidwawo, masikuwo adzafupikitsidwa."
|
neutral
|
Kapena ali nawo makutu omvelera?
|
neutral
|
Solomo anali munthu wolemera kwambiri.
|
neutral
|
Mukuona bwanji ngati ndili ndi umboni wowonekera wochokera kwa Mbuye wanga, ndipo nkundipatsa rizq labwino (lahalali) lochokera kwa Iye, (ndisiye zimenezi ndi kusankha njira yokhota)?
|
neutral
|
Inu Munafuna kuzizindikiritsa Nokha kwa wanthu; choncho, kupyolera mwa liu lapakamwa panu munadzetsa chilengedwe ndi kupanga m'mwamba.
|
neutral
|
Iwo ayenera kuti anaphunzitsa mwana wawo, dzina lake Samisoni, chilamulo cha Mulungu ndipo zotsatira zake zinali zabwino.
|
neutral
|
Ndipo wawakonzera minda yomwe mitsinje ikuyenda pansi (ndi pasogolo) pake, adzakhala m'menemo muyaya.
|
neutral
|
Ndipo adzabwerera kwa anthu ake
|
neutral
|
Ndithu Allah ndi mwini kuthekera, komanso muwongoli ku njira ya chiongoko.
|
neutral
|
Uthenga wabwino wa Ufumu ukulalikidwa padziko lonse lapansi monga mmene Yesu ananenera.
|
neutral
|
Ndikuganiza kuti ukunena zowona, Tim!
|
joy
|
Mose ankakonda Mulungu komanso aisiraeli anzake.
|
disgust
|
Chifukwa chake, anthu ammudziwo adampatsa dzina losavuta ndi lalifupi - Philip Goldson.
|
neutral
|
" (Iwo) adati: "Kodi watidzera kuti utichotse ku zimene tidawapeza nazo makolo athu kuti ukulu ukhale wa inu awiri m'dzikoli?
|
neutral
|
Koma yemwe akwaniritse Zomwe adalonjeza kwa Mulungu, amulipira malipiro aakulu.
|
neutral
|
Mukuona bwanji ngati ndili ndi chisonyezo choonekera chochokera kwa Mbuye wanga (chosonyeza kuona kwa zimenezi), nandipatsanso chifundo chochokera kwa Iye.
|
neutral
|
Inatengedwanso ndi Nigerian Bulletin.
|
neutral
|
"Pamene m'bale wawo Swalih adawauza kuti: "Kodi simuopa (Allah)?"
|
fear
|
Anthu ake adamuuza: "usanyade, ndithu Allah sakonda onyada."
|
anger
|
Koma pamene Aigupto analondola Aisrayeliwo m'nyanjamo, Mulungu anabwezeretsa madziwo m'malo mwake.
|
anger
|
Ndipo adzafika kwa anthu n'kumawaitanira anthuwo ku zofuna zake,
|
anger
|
Uku iwo akuyang'ana zomwe amawachitira Okhulupirira, (pootchedwa ndi moto).
|
disgust
|
Bukuli lidzasintha malingaliro anu. "
|
neutral
|
Subsets and Splits
No community queries yet
The top public SQL queries from the community will appear here once available.